Francais | English | Espanõl

Mlungu dalitsani Malawi

From Wikipedia, the free encyclopedia

Jump to: navigation, search

Mulungu dalitsa Malawi is the national anthem of Malawi. It was composed by Michael-Fredrick Paul Sauka, who also wrote the words. It was adopted in 1964 as a result of a competition.

Mulungu dalitsa malawi Translated as "God Bless Malawi"

Mulungu dalitsa Malawi,

Mumsunge m'mtendere.

Gonjetsani adani onse,

Njala, nthenda, nsanje.

Lunzitsani mitima yathu,

Kuti tisaope.

Mdalitse Mtsogo leri nafe,

Ndi Mayi Malawi.

Malawi ndziko lokongola,

La chonde ndi ufulu,

Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,

Ndithudi tadala.

Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,

N'mphatso zaulere.

Nkhalango, madambo abwino.

Ngwokoma Malawi.

O Ufulu tigwirizane,

Kukweza Malawi.

Ndi chikondi, khama, kumvera,

Timutumikire.

Pa nkhondo nkana pa mtendere,

Cholinga n'chimodzi.

Mai, bambo, tidzipereke,

Pokweza Malawi.

O God bless our land of Malawi,

Keep it a land of peace.

Put down each and every enemy,

Hunger, disease, envy.

Join together all our hearts as one,

That we be free from fear.

Bless our leader,

each and every one,

And Mother Malawi.

Our own Malawi, this land so fair,

Fertile and brave and free.

With its lakes, refreshing mountain air,

How greatly blest are we.

Hills and valleys, soil so rich and rare

Give us a bounty free.

Wood and forest, plains so broad and fair,

All - beauteous Malawi.

Freedom ever, let us all unite

To build up Malawi.

With our love, our zeal and loyalty,

Bringing our best to her.

In time of war, or in time of peace,

One purpose and one goal.

Men and women serving selflessly

In building Malawi.

[edit] External links

Image:Nationalsångsstub.png This national, regional or organisational anthem-related article is a stub. You can help Wikipedia by expanding it.
ny:Mlungu dalitsani Malaŵi

de:Mlungu salitsani malawi es:Mlungu dalitsani Malawi nl:Mlungu dalitsani Malawi no:Mlungu dalitsani Malawi pt:Hino nacional do Malawi fi:Mlungu salitsani malawi

Personal tools